Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Zekariya 6:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo ndinayankha ndinati kwa mthenga wolankhula ndi ine, Izi nziyani, mbuyanga?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo ndinayankha ndinati kwa mthenga wolankhula ndi ine, Izi nziyani, mbuyanga?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Tsono ndidafunsa mngelo amene ndinkalankhula naye uja kuti, “Mbuye wanga, kodi zimenezi zikutanthauza chiyani?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Ndinafunsa mngelo amene amayankhula nane uja kuti, “Kodi mbuye wanga chimenechi nʼchiyani?”

Onani mutuwo Koperani




Zekariya 6:4
5 Mawu Ofanana  

Pamenepo ndinati, Awa ndi chinai, mbuyanga? Ndi mthenga wakulankhula ndi ine anati kwa ine, Ndidzakuonetsa awa ndi chiyani.


Ndipo ndinayankha ndi kunena ndi mthenga wakulankhula ndi ine, ndi kuti, Izi nziyani mbuyanga?


Ndipo ndinati kwa mthenga wakulankhula ndi ine, Amenewa amuka naye kuti efayo?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa