Zekariya 6:2 - Buku Lopatulika2 Ku galeta woyamba kunali akavalo ofiira; ndi kugaleta wachiwiri akavalo akuda; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ku galeta woyamba kunali akavalo ofiira; ndi kugaleta wachiwiri akavalo akuda; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Galeta loyamba linkakokedwa ndi akavalo ofiira, lachiŵiri akavalo akuda, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Galeta loyamba limakokedwa ndi akavalo ofiira, lachiwiri ndi akavalo akuda, Onani mutuwo |