Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Zekariya 5:7 - Buku Lopatulika

7 ndipo taonani, chozunguniza chantovu chotukulidwa: ndipo ichi ndi mkazi wokhala pakati pa efa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 ndipo taonani, chozunguniza chantovu chotukulidwa: ndipo ichi ndi mkazi wokhala pakati pa efa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Chovundikira chake chinali chamtovu, ndipo chitatukuka, ndidaona mkazi atakhala tsonga m'gondolomo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Pamenepo chovundikira chake chamtovu chinatukulidwa, ndipo mʼdengumo munali mutakhala mkazi.

Onani mutuwo Koperani




Zekariya 5:7
11 Mawu Ofanana  

Katundu wa Babiloni, amene anamuona Yesaya mwana wa Amozi.


Katundu wa Mowabu. Pakuti usiku umodzi Ari wa ku Mowabu wapasuka, nakhala chabe; usiku umodzi Kiri wa Mowabu wapasuka, nakhala chabe.


Inu munapanganso chosungamo madzi a thamanda lakale, pakati pa malinga awiri; koma inu simunamuyang'ane iye amene anachichita icho, ngakhale kusamalira iye amene analipanga kale.


Ndipo wakuima pakati pa mitengo yamchisu anayankha, nati, Awa ndiwo amene Yehova anawatumiza ayendeyende m'dziko.


Ndipo ndinati, Nchiyani ichi? Nati iye, Ichi ndi efa alikutuluka. Natinso, Ichi ndi maonekedwe ao m'dziko lonse;


Ndipo anati, Uyu ndi uchimo; namgwetsa m'kati mwa efa; naponya ntovu wolemerawo pakamwa pake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa