Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Zekariya 5:1 - Buku Lopatulika

1 Pamenepo ndinakwezanso maso anga, ndinapenya, taonani, mpukutu wouluka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Pamenepo ndinakwezanso maso anga, ndinapenya, taonani, mpukutu wouluka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Ndidaonanso zinthu zina m'masomphenya: ndidaona chikalata chofutukula chikuuluka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Ndinayangʼananso ndipo taonani ndinaona chikalata chimene chimawuluka.

Onani mutuwo Koperani




Zekariya 5:1
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anati kwa ine, Tenga iwe polembapo papakulu, nulembe pamenepo ndi malembedwe odziwika, Kangazakufunkha Fulumirakusakaza.


Ndipo anati kwa ine, Uona chiyani? Ndipo ndinayankha, Ndiona mpukutu wouluka; utali wake mikono makumi awiri, ndi chitando chake mikono khumi.


ndipo anali nako m'dzanja lake kabuku kofunyulula: ndipo anaponda nalo phazi lake lamanja panyanja, ndi lamanzerelo pamtunda,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa