Zekariya 4:14 - Buku Lopatulika14 Pamenepo anati, Awa ndi ana aamuna awiri a mafuta oimirira pamaso pa Mbuye wa dziko lonse lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pamenepo anati, Awa ndi ana amuna awiri a mafuta oimirira pamaso pa Mbuye wa dziko lonse lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Tsono iye adati, “Ameneŵa ndi anthu aŵiri odzozedwa aja, amene amatumikira Chauta, Ambuye a dziko lonse lapansi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Choncho iye anati, “Amenewa ndi anthu awiri amene adzozedwa kuti atumikire Ambuye pa dziko lonse lapansi.” Onani mutuwo |