Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Zekariya 4:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo anandiyankha, nati, Sudziwa kodi kuti nziyani izi? Ndipo ndinati, Iai, mbuyanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo anandiyankha, nati, Sudziwa kodi kuti nziyani izi? Ndipo ndinati, Iai, mbuyanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Iye adati, “Monga iwe zimenezi sukuzidziŵa?” Ine ndidayankha kuti, “Inde, mbuye wanga, sindikuzidziŵa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Iye anandiyankha kuti, “Kodi iwe sukuzidziwa zimenezi?” Ine ndinati, “Ayi mbuye wanga.”

Onani mutuwo Koperani




Zekariya 4:13
4 Mawu Ofanana  

Ndipo ndinayankha kachiwiri, ndinati naye, Nzotani nthambi ziwiri izi za azitona zilikutsanula zokha mafuta onga golide mwa misiwe iwiri yagolide?


Ndipo ndinayankha ndi kunena ndi mthenga wakulankhula ndi ine, ndi kuti, Izi nziyani mbuyanga?


Ndipo mthenga wakulankhula ndi ine anayankha, nati kwa ine, Sudziwa kodi kuti nziyani izi? Ndipo ndinati, Iai, mbuyanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa