Zekariya 4:3 - Buku Lopatulika3 ndi mitengo iwiri ya azitona pomwepo, wina kudzanja lamanja la mbaleyo, ndi wina kudzanja lake lamanzere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 ndi mitengo iwiri ya azitona pomwepo, wina kudzanja lamanja la mbaleyo, ndi wina kudzanja lake lamanzere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pambali pake pa choikaponyalecho pali mitengo iŵiri ya olivi, wina ku dzanja lamanja, wina ku dzanja lamanzere.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ndiponso pambali pake pali mitengo ya olivi iwiri, umodzi uli kumanja kwa mbaleyo ndipo winawo kumanzere.” Onani mutuwo |