Zekariya 2:6 - Buku Lopatulika6 Haya, haya, thawani kudziko la kumpoto ati Yehova; pakuti ndinakubalalitsani ngati mphepo zinai za kuthambo, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Haya, haya, thawani kudziko la kumpoto ati Yehova; pakuti ndinakubalalitsani ngati mphepo zinai za kuthambo, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Chauta akunena kuti, “Tiyeni, tiyeni, thaŵaniko ku dziko lakumpoto. Paja ndidakumwazirani ku mphepo zinai za mlengalenga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 “Tulukani! Tulukani! Thawaniko ku dziko la kumpoto,” akutero Yehova, “pakuti ndinakumwazirani ku mphepo zinayi zamlengalenga,” akutero Yehova. Onani mutuwo |