Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Zekariya 12:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo kudzachitika tsiku lomwelo, ndidzayesa kuononga amitundu onse akudza kuyambana ndi Yerusalemu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo kudzachitika tsiku lomwelo, ndidzayesa kuononga amitundu onse akudza kuyambana ndi Yerusalemu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Tsiku limenelo ndidzaononga mitundu yonse ya anthu yofuna kuthira nkhondo Yerusalemu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Pa tsiku limenelo ndidzawononga mitundu yonse yofuna kuthira nkhondo Yerusalemu.

Onani mutuwo Koperani




Zekariya 12:9
6 Mawu Ofanana  

Ndipo khamu la mitundu yonse yomenyana ndi Ariyele, ngakhale yonse yomenyana naye ndi linga lake, ndi kumsautsa idzafanana ndi loto, masomphenya a usiku.


Taona, iwo angasonkhanitse pamodzi, koma si ndi Ine; aliyense amene adzasonkhana pamodzi akangane ndi iwe adzagwa chifukwa cha iwe.


Palibe chida chosulidwira iwe chidzapindula; ndipo lilime lonse limene lidzakangana nawe m'chiweruzo udzalitsutsa. Ichi ndi cholowa cha atumiki a Yehova, ndi chilungamo chao chimene chifuma kwa Ine, ati Yehova.


ndipo ndidzagubuduza mipando yachifumu ya maufumu, ndidzaononga mphamvu ya maufumu a amitundu; ndidzagubuduza magaleta ndi iwo akuyendapo; ndi akavalo ndi apakavalo adzatsika, yense ndi lupanga la mbale wake.


Taonani, ndidzaika Yerusalemu akhale chipanda chodzandiritsa kwa mitundu yonse ya anthu yozungulirapo, ndipo chidzafikira Yuda yemwe pomangira misasa Yerusalemu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa