Zekariya 12:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo Yehova adzayamba kupulumutsa mahema a Yuda, kuti ulemerero wa nyumba ya Davide ndi ulemerero wa okhala mu Yerusalemu usakulire Yuda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo Yehova adzayamba kupulumutsa mahema a Yuda, kuti ulemerero wa nyumba ya Davide ndi ulemerero wa okhala m'Yerusalemu usakulire Yuda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 “Chauta adzayamba wapulumutsa mahema onse a ku Yuda, kuti ulemerero wonse wa banja la Davide ndi wa anthu a ku Yerusalemu usapambane ulemerero wa Yuda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 “Yehova adzapulumutsa malo okhala Yuda poyamba, kuti ulemu wa nyumba ya Davide ndi wa anthu okhala mu Yerusalemu usapambane ulemu wa Yuda. Onani mutuwo |