Zekariya 12:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo akalonga a Yuda adzanena m'mtima mwao, Okhala mu Yerusalemu ndiwo mphamvu yanga mu Yehova wa makamu Mulungu wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo akalonga a Yuda adzanena m'mtima mwao, Okhala m'Yerusalemu ndiwo mphamvu yanga m'Yehova wa makamu Mulungu wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pamenepo atsogoleri a Yuda adzavomera kuti, ‘Indedi, anthu a ku Yerusalemu amapeza mphamvu mwa Chauta Wamphamvuzonse, Mulungu wao.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pamenepo atsogoleri a Yuda adzayankhula mʼmitima mwawo kuti, ‘Anthu a ku Yerusalemu ndi amphamvu, chifukwa Yehova Wamphamvuzonse ndiye Mulungu wawo.’ Onani mutuwo |