Zekariya 12:4 - Buku Lopatulika4 Tsiku ilo, ati Yehova, ndidzakantha kavalo aliyense ndi kumdabwitsa, ndi womkwera adzayaluka; ndipo ndidzatsegulira maso anga nyumba ya Yuda, ndi kukantha kavalo aliyense wa mitundu ya anthu akhale wakhungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Tsiku ilo, ati Yehova, ndidzakantha kavalo aliyense ndi kumdabwitsa, ndi womkwera adzayaluka; ndipo ndidzatsegulira maso anga nyumba ya Yuda, ndi kukantha kavalo aliyense wa mitundu ya anthu akhale wakhungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Chauta akunena kuti, “Tsiku limenelo kavalo aliyense ndidzamchititsa mantha osokonezeka nawo, ndipo wokwerapo wake adzachita msala. Banja la Yuda ndidzaliyang'anira, koma akavalo a adani ao onse ndidzaŵachititsa khungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Pa tsiku limenelo kavalo aliyense ndidzamuchititsa mantha kuti asokonezeke, ndipo wokwerapo wake ndidzamuchititsa misala,” akutero Yehova. “Ndidzayangʼanira nyumba ya Yuda koma ndidzachititsa khungu akavalo onse a anthu a mitundu ina. Onani mutuwo |