Zekariya 11:9 - Buku Lopatulika9 Pamenepo ndinati, Sindidzadyetsanso inu; chilikufa chife; chosoweka chisoweke; ndi zotsala zidyane, chonse nyama ya chinzake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pamenepo ndinati, Sindidzadyetsanso inu; chilikufa chife; chosoweka chisoweke; ndi zotsala zidyane, chonse nyama ya chinzake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tsono ndidauza gulu la nkhosa lija kuti, “Sindidzakuŵetaninso. Imene ikuti ife, ife basi. Imene ikuti isokere, isokere, ndipo otsalanu, muzidyana.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndinawuza gulu la nkhosalo kuti, “Sindidzakhalanso mʼbusa wanu. Imene ikufa, ife, ndipo imene ikuwonongeka, iwonongeke, zimene zatsala zizidyana.” Onani mutuwo |