Zekariya 11:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo ndinatha abusa atatuwo mwezi umodzi; pakuti mtima wanga unalema nao, ndi mtima waonso unaipidwa nane. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo ndinatha abusa atatuwo mwezi umodzi; pakuti mtima wanga unalema nao, ndi mtima waonso unaipidwa nane. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Pa mwezi umodzi ndidachotsa abusa atatu aja. Adafika pondipsetsa mtima, ine osathanso kuŵapirira. Iwonso adadana nane. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Pa mwezi umodzi ndinachotsa abusa atatu. Abusawo anadana nane, ndipo ndinatopa nawo. Onani mutuwo |