Zekariya 11:4 - Buku Lopatulika4 Atero Yehova Mulungu wanga: Dyetsani zoweta zakukaphedwa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Atero Yehova Mulungu wanga: Dyetsani zoweta zakukaphedwa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Chauta, Mulungu wanga, adandiwuza kuti, “Ŵeta bwino nkhosa zimene zili kukaphedwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Yehova Mulungu wanga akuti, “Dyetsa nkhosa zimene zikukaphedwa. Onani mutuwo |