Zekariya 11:3 - Buku Lopatulika3 Mau a kuchema kwa abusa! Pakuti ulemerero wao waipsidwa; mau a kubangula kwa misona ya mikango! Pakuti kudzikuza kwa Yordani kwaipsidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mau a kuchema kwa abusa! Pakuti ulemerero wao waipsidwa; mau a kubangula kwa misona ya mikango! Pakuti kudzikuza kwa Yordani kwaipsidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Imvani abusa, nawonso akulira mokweza, pakuti mabusa ao obiriŵira auma. Imvani misona ya mikango ikubangula, pakuti nkhalango yoŵirira ya ku Yordani aiyeretsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Imvani kulira mwachisoni kwa abusa; msipu wawo wobiriwira wawonongeka! Imvani kubangula kwa mikango; nkhalango yowirira ya ku Yorodani yawonongeka! Onani mutuwo |