Zekariya 10:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo adzakhala ngati ngwazi zakupondereza adani m'thope la kubwalo kunkhondo; ndipo adzachita nkhondo, chifukwa Yehova ali nao; ndi apakavalo adzachitidwa manyazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo adzakhala ngati ngwazi zakupondereza adani m'thope la kubwalo kunkhondo; ndipo adzachita nkhondo, chifukwa Yehova ali nao; ndi apakavalo adzachitidwa manyazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ayuda onse pamodzi adzakhala ngati ngwazi zankhondo, zopondereza adani m'matope am'miseu nthaŵi yankhondo. Adzamenya nkhondo chifukwa choti Chauta ali nawo, ndipo adzagonjetsa adani okwera pa akavalo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Onse pamodzi adzakhala ngati ngwazi zankhondo zoponda mʼmatope a mʼmisewu nthawi yankhondo. Chifukwa Yehova adzakhala nawo, adzachita nkhondo ndi kugonjetsa okwera pa akavalo. Onani mutuwo |