Zekariya 10:1 - Buku Lopatulika1 Pemphani kwa Yehova mvula, m'nyengo ya mvula ya masika, kwa Yehova wolenga mphezi; ndipo adzawapatsa mivumbi ya mvula, kwa yense zophukira kuthengo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Pemphani kwa Yehova mvula, m'nyengo ya mvula ya masika, kwa Yehova wolenga mphezi; ndipo adzawapatsa mivumbi ya mvula, kwa yense zophukira kuthengo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pemphani Chauta kuti akupatseni mvula pa nyengo yobzala. Ndiye amene amapanga mitambo yamvula. Ndiye amene amagwetsera anthu mvula yamvumbi, ndiye amene amameretsera aliyense mbeu m'munda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Pemphani mvula kwa Yehova pa nthawi yamphukira; ndi Yehova amene amapanga mitambo ya mvula. Iye amagwetsa mivumbi ya mvula kwa anthu, ndi kumeretsa mbewu za mʼmunda kwa aliyense. Onani mutuwo |