Zekariya 9:17 - Buku Lopatulika17 Pakuti ukoma wake ndi waukulu ndithu, ndi kukongola kwake nkwakukulu ndithu! Tirigu adzakometsera anyamata, ndi vinyo watsopano anamwali. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Pakuti ukoma wake ndi waukulu ndithu, ndi kukongola kwake nkwakukulu ndithu! Tirigu adzakometsera anyamata, ndi vinyo watsopano anamwali. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Dzikolo lidzakhaladi lokongola kwambiri. Tirigu adzalimbitsa anyamata, ndipo vinyo watsopano adzakometsa anamwali. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Taonani chikoka ndi kukongola kwawo! Tirigu adzasangalatsa anyamata, ndi vinyo watsopano anamwali. Onani mutuwo |