Zefaniya 3:9 - Buku Lopatulika9 Pakuti pamenepo ndidzapatsa mitundu ya anthu mlomo woyera, kuti onsewa aitanire pa dzina la Yehova kumtumikira ndi mtima umodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pakuti pamenepo ndidzapatsa mitundu ya anthu mlomo woyera, kuti onsewa aitanire pa dzina la Yehova kumtumikira ndi mtima umodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 “Pamenepo ndidzasintha malankhulidwe a mitundu yonse, nkuŵapatsa malankhulidwe abwino, kuti onse azitama dzina la Chauta mopemba ndi kumamtumikira mogwirizana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Pamenepo ndidzayeretsa milomo ya anthu a mitundu yonse kuti anthu onsewo ayitane dzina la Yehova ndi kumutumikira Iye pamodzi. Onani mutuwo |