Zefaniya 3:10 - Buku Lopatulika10 Kuchokera tsidya lija la mitsinje ya Kusi ondipembedza, ndiwo mwana wamkazi wa obalalika anga, adzabwera nacho chopereka changa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Kuchokera tsidya lija la mitsinje ya Kusi ondipembedza, ndiwo mwana wamkazi wa obalalika anga, adzabwera nacho chopereka changa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ngakhale kutali kutsidya kwa mitsinje ya ku Etiopiya, anthu ondipembedza, anthu anga obalalika, adzapereka nsembe kwa Ine.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Kuchokera kutsidya kwa mitsinje ya ku Kusi anthu anga ondipembedza, omwazikana, adzandibweretsera zopereka. Onani mutuwo |