Zefaniya 3:7 - Buku Lopatulika7 Ndinati, Zedi udzandiopa Ine, udzalola kulangizidwa, kuti pokhala pake pasaonongeke, monga mwa zonse ndamuikira; koma analawirira mamawa, navunditsa machitidwe ao onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndinati, Zedi udzandiopa Ine, udzalola kulangizidwa, kuti pokhala pake pasaonongeke, monga mwa zonse ndamuikira; koma analawirira mamawa, navunditsa machitidwe ao onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ndidaaganiza kuti ndithudi anthu anga andiwopa, kuti avomera malango anga, ndipo kuti saiŵala malamulo anga. Koma ndi pamene iwo adanyanyira kumachita zoipa pa zochita zao zonse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndinati, ‘Ndithudi, anthu a mu mzindawu adzandiopa ndi kumvera kudzudzula kwanga!’ Ndipo sindidzawononga nyumba zawo, kapena kuwalanganso. Koma iwo anali okonzeka kuchita mwachinyengo zinthu zonse zimene amachita. Onani mutuwo |