Zefaniya 3:6 - Buku Lopatulika6 Ndaononga amitundu; nsanja zao za kungodya nza bwinja, ndapasula miseu yao, palibe wopitapo; mizinda yao yaonongeka, palibe munthu, palibe wokhalamo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndaononga amitundu; nsanja zao za kungodya nza bwinja, ndapasula miseu yao, palibe wopitapo; midzi yao yaonongeka, palibe munthu, palibe wokhalamo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Chauta akuti, “Ndaononga mitundu yonse ya anthu ndipo malinga ao onse ankhondo ndaŵaphwasula. Miseu yao ndaifafaniza palibenso anthu oyendamo. Mizinda yao yachitika bwinja, mulibe munthu ndi mmodzi yemwe wotsalamo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 “Ndachotseratu mitundu ya anthu; ndagwetsa malinga awo. Ndipo sindinasiye ndi mmodzi yemwe mʼmisewu mwawo, popanda aliyense wodutsa. Mizinda yawo yawonongedwa; palibe aliyense adzatsalemo. Onani mutuwo |