Zefaniya 3:5 - Buku Lopatulika5 Yehova pakati pake ali wolungama; sadzachita chosalungama, m'mawa ndi m'mawa aonetsera chiweruzo chake poyera, chosasowa kanthu; koma wosalungama sadziwa manyazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Yehova pakati pake ali wolungama; sadzachita chosalungama, m'mawa ndi m'mawa aonetsera chiweruzo chake poyera, chosasowa kanthu; koma wosalungama sadziwa manyazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Koma Chauta ndi wolungama mumzindamo, Iyeyo salakwa. Amaweruza molungama tsiku ndi tsiku, nthaŵi zonse salephera, koma osalungama akuchitabe zoipa opanda manyazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Yehova amene ali pakati pawo ndi wolungama; Iye salakwa. Tsiku ndi tsiku amaweruza molungama, ndipo tsiku lililonse salephera, komabe ochita zoyipa sachita manyazi nʼkomwe. Onani mutuwo |