Zefaniya 3:4 - Buku Lopatulika4 Aneneri ake ndiwo anthu a matukutuku ndi onyenga; ansembe ao anaipsa malo opatulika, napotoza chilamulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Aneneri ake ndiwo anthu a matukutuku ndi onyenga; ansembe ao anaipsa malo opatulika, napotoza chilamulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Aneneri ake anali achabechabe, anthu osakhulupirika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Aneneri ake ndi odzikuza; anthu achinyengo. Ansembe ake amadetsa malo opatulika ndipo amaphwanya lamulo. Onani mutuwo |