Zefaniya 3:13 - Buku Lopatulika13 Otsala a Israele sadzachita chosalungama, kapena kunena mabodza; ndi m'kamwa mwao simudzapezeka lilime lonyenga; pakuti adzadya nadzagona pansi, ndi palibe wakuwaopsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Otsala a Israele sadzachita chosalungama, kapena kunena mabodza; ndi m'kamwa mwao simudzapezeka lilime lonyenga; pakuti adzadya nadzagona pansi, ndi palibe wakuwaopsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Otsala a mu Israeleŵa sadzalakwanso, sadzalankhulanso zabodza, sadzachitanso zonyenga, Adzakhala pabwino mwamtendere, popanda wina woŵaopsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Aisraeli otsala sadzachitanso zolakwika; sadzayankhulanso zonama, ngakhale chinyengo sichidzatuluka mʼkamwa mwawo. Adzadya ndi kugona ndipo palibe amene adzawachititse mantha.” Onani mutuwo |