Zefaniya 3:12 - Buku Lopatulika12 Koma ndidzasiya pakati pako anthu ozunzika ndi osauka, ndipo iwo adzakhulupirira dzina la Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Koma ndidzasiya pakati pako anthu ozunzika ndi osauka, ndipo iwo adzakhulupirira dzina la Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Pakati panu ndidzasiya anthu odzichepetsa ndi otsika. Iwowo adzafunafuna populumukira m'dzina la Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Koma ndidzasiya pakati panu anthu ofatsa ndi odzichepetsa, amene amadalira dzina la Yehova. Onani mutuwo |