Zefaniya 2:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo adzatambasulira dzanja lake kumpoto nadzaononga Asiriya, nadzasanduliza Ninive akhale bwinja, wouma ngati chipululu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo adzatambasulira dzanja lake kumpoto nadzaononga Asiriya, nadzasanduliza Ninive akhale bwinja, wouma ngati chipululu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Chauta adzasamulira dzanja lake kumpoto ndi kuwononga dziko la Asiriya. Mzinda wa Ninive adzausandutsa bwinja, udzakhala wagwaa ngati chipululu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Yehova adzatambasulira dzanja lake kumpoto ndi kuwononga Asiriya, kusiya Ninive atawonongekeratu ndi owuma ngati chipululu. Onani mutuwo |