Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Zefaniya 2:12 - Buku Lopatulika

12 Inunso Akusi, mudzaphedwa ndi lupanga langa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Inunso Akusi, mudzaphedwa ndi lupanga langa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Inunso Aetiopiya, Chauta adzakukanthani ndi lupanga lake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 “Inunso anthu a ku Kusi, mudzaphedwa ndi lupanga.”

Onani mutuwo Koperani




Zefaniya 2:12
12 Mawu Ofanana  

Ukani Yehova, Mumtsekereze, mumgwetse, landitsani moyo wanga kwa woipa ndi lupanga lanu;


Iwe Asiriya chibonga cha mkwiyo wanga, ndodo m'dzanja lake muli ukali wanga!


Achokera m'dziko lakutali, kumalekezero a thambo, ngakhale Yehova, ndi zida za mkwiyo wake, kuti aononge dziko lonse.


Ndipo Yehova anati, Monga mtumiki wanga Yesaya wayenda maliseche ndi wopanda nsapato zaka zitatu, akhale chizindikiro ndi chodabwitsa kwa Ejipito ndi kwa Etiopiya;


Chifukwa kuti Ine ndine Yehova Mulungu wako, Woyera wa Israele, Mpulumutsi wako; ndapatsa Ejipito dombolo lako, Etiopiya ndi Seba m'malo mwako.


Ndipo ndidzalimbitsa manja a mfumu ya ku Babiloni, ndi kuika lupanga langa m'dzanja lake; koma ndidzathyola manja a Farao, ndipo adzabuula pamaso pake mabuulo a munthu wopyozedwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa