Zefaniya 2:11 - Buku Lopatulika11 Yehova adzawakhalira woopsa; pakuti adzaondetsa milungu yonse ya padziko lapansi; ndipo adzamlambira Iye, yense pamalo pake, a m'zisumbu zonse za amitundu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Yehova adzawakhalira woopsa; pakuti adzaondetsa milungu yonse ya pa dziko lapansi; ndipo adzamlambira Iye, yense pamalo pake, a m'zisumbu zonse za amitundu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Motero Chauta adzaŵaopsa kwambiri. Adzaononga milungu yonse ya pa dziko lapansi. Mitundu yonse ya anthu idzampembedza Chauta, mtundu uliwonse ku dziko lakwao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Yehova adzawachititsa mantha kwambiri pamene adzawononga milungu yonse ya mʼdzikomo. Ndipo mitundu ya anthu pa dziko lonse idzamulambira, uliwonse ku dziko la kwawo. Onani mutuwo |