Zefaniya 2:10 - Buku Lopatulika10 Ichi adzakhala nacho m'malo mwa kudzikuza kwao, chifukwa anatonza, nadzikuza pa anthu a Yehova wa makamu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ichi adzakhala nacho m'malo mwa kudzikuza kwao, chifukwa anatonza, nadzikuza pa anthu a Yehova wa makamu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Chimenechi chidzakhala chilango choyenerera kunyada kwaoko, chifukwa adanyoza anthu a Chauta Wamphamvuzonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ichi ndi chimene adzalandire chifukwa cha kunyada kwawo, chifukwa chonyoza ndi kuchitira chipongwe anthu a Yehova Wamphamvuzonse. Onani mutuwo |