Zefaniya 1:7 - Buku Lopatulika7 Khala chete pamaso pa Ambuye Yehova; pakuti tsiku la Yehova liyandikira; pakuti Yehova wakonzeratu nsembe, anapatula oitanidwa ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Khala chete pamaso pa Ambuye Yehova; pakuti tsiku la Yehova liyandikira; pakuti Yehova wakonzeratu nsembe, anapatula oitanidwa ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Khalani chete pamaso pa Ambuye Chauta! Tsikutu la Chauta layandikira. Chauta wakonza kuti anthu ake adzaperekedwe ngati nsembe, ndipo wapatuliratu oitanidwa odzapereka nsembeyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Khalani chete pamaso pa Ambuye Yehova, chifukwa tsiku la Yehova layandikira. Yehova wakonzekera kupereka nsembe; wapatula iwo amene wawayitana. Onani mutuwo |