Zefaniya 1:6 - Buku Lopatulika6 ndi iwo akubwerera osamtsata Yehova; ndi osamfuna Yehova, kapena kufunsira kwa Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ndi iwo akubwerera osamtsata Yehova; ndi osamfuna Yehova, kapena kufunsira kwa Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Iwowo adafulatira Chauta osamtsatanso, safuna kupembedza Chauta, kapena kumpempha nzeru.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 amene abwerera mʼmbuyo osatsata Yehova, osafunafuna kapena kupempha nzeru kwa Yehova. Onani mutuwo |