Zefaniya 1:5 - Buku Lopatulika5 ndi iwo akulambira khamu la kumwamba pamwamba pa matsindwi; ndi iwo akulambira, akulumbira pali Yehova, nalumbiranso pali mfumu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 ndi iwo akulambira khamu la kumwamba pamwamba pa matsindwi; ndi iwo akulambira, akulumbira pali Yehova, nalumbiranso pali mfumu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndidzafafanizanso amene amaŵerama pa madenga ao nkumapembedza dzuŵa, mwezi ndi nyenyezi. Ndidzaononganso amene amati kwinaku akulambira Chauta ndi kulumbira m'dzina lake, kwinaku nkumalumbira m'dzina la Milikomu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 amene amagwada pa madenga a nyumba zawo kupembedza zolengedwa zamumlengalenga, amene amagwada ndi kulumbira mʼdzina la Yehova, komanso mʼdzina la Moleki, Onani mutuwo |