Zefaniya 1:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo zolemera zao zidzakhala zakufunkhidwa; ndi nyumba zao zabwinja; adzamangadi nyumba, koma sadzagonamo; adzaoka minda yampesa koma sadzamwa vinyo wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo zolemera zao zidzakhala zakufunkhidwa; ndi nyumba zao zabwinja; adzamangadi nyumba, koma sadzagonamo; adzaoka minda yampesa koma sadzamwa vinyo wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Anthu otereŵa chuma chao adani adzachifunkha, nyumba zao adzaziphwasula. Adzamanga nyumba, koma sadzakhalamo. Adzabzala mphesa, koma sadzamwa vinyo wake.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Chuma chawo chidzafunkhidwa, nyumba zawo zidzagwetsedwa. Adzamanga nyumba, koma osakhalamo; adzadzala minda ya mpesa koma sadzamwako vinyo wake.” Onani mutuwo |