Zefaniya 1:14 - Buku Lopatulika14 Tsiku lalikulu la Yehova lili pafupi, lili pafupi lifulumira kudza, mau a tsiku la Yehova; munthu wamphamvu adzalirapo mowawa mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Tsiku lalikulu la Yehova lili pafupi, lili pafupi lifulumira kudza, mau a tsiku la Yehova; munthu wamphamvu adzalirapo mowawa mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Tsiku lalikulu la Chauta lili pafupi, layandikira ndipo likudza mofulumira. Tsikulo kubwera kwake nkopweteka, ngakhale ankhondo amphamvu omwe akulira pamenepo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Tsiku lalikulu la Yehova layandikira, layandikira ndipo lifika msanga. Tamverani! Kulira kwa pa tsiku la Yehova kudzakhala kowawa, ngakhale munthu wolimba mtima adzalira kwambiri. Onani mutuwo |