Zefaniya 1:11 - Buku Lopatulika11 Chemani okhala m'chigwa, pakuti amalonda onse atayika, onsewo osenza siliva aonongeka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Chemani okhala m'chigwa, pakuti amalonda onse atayika, onsewo osenza siliva aonongeka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Inu okhala ku chigwa cha mzinda lirani komvetsa chisoni, chifukwa amalonda onse atha, onse ogulitsa siliva aonongeka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Lirani mwachisoni, inu amene mumakhala kumene kuli msika; a malonda anu onse adzapululidwa, ndiponso onse amene ali ndi siliva adzawonongedwa. Onani mutuwo |