Zefaniya 1:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo tsiku ilo, ati Yehova, kudzakhala phokoso lakulira lochokera ku Chipata cha Nsomba, ndi kuchema kochokera kudera lachiwiri, ndi kugamuka kwakukulu kochokera kuzitunda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo tsiku ilo, ati Yehova, kudzakhala phokoso lakulira lochokera kuchipata chansomba, ndi kuchema kochokera kudera lachiwiri, ndi kugamuka kwakukulu kochokera kuzitunda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Chauta akunena kuti, “Pa tsiku limenelo kulira kwakukulu kudzamveka ku Chipata cha Msika wa Nsomba; kulira kwakukuluko kudzamveka ku chigawo cham'kati cha mzinda wa Yerusalemu; kudzamvekanso kugunda kuchokera ku mapiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 “Pa tsiku limenelo,” akutero Yehova, “Kufuwula kwakukulu kudzamveka pa Chipata cha Nsomba, kulira kwa chisoni kuchokera mʼChigawo Chatsopano, ndi phokoso la kugumuka kochokera ku mapiri. Onani mutuwo |