Yuda 1:8 - Buku Lopatulika8 Momwemonso iwo m'kulota kwao adetsa matupi ao, napeputsa ufumu, nachitira mwano maulemerero. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Momwemonso iwo m'kulota kwao adetsa matupi ao, napeputsa ufumu, nachitira mwano maulemerero. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Komabe anthu ameneŵa akuchita chimodzimodzi. Potsata maloto ao, amaipitsa matupi ao, amakana ulamuliro wa Mulungu, ndipo amachita chipongwe aulemerero a Kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Nʼchimodzimodzinso zimene akuchita anthu amenewa potsata maloto awo, amadetsa matupi awo, amakana ulamuliro wa Mulungu ndiponso amachitira chipongwe angelo akumwamba. Onani mutuwo |