Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yoweli 3:20 - Buku Lopatulika

20 Koma Yuda adzakhala chikhalire, ndi Yerusalemu ku mibadwomibadwo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Koma Yuda adzakhala chikhalire, ndi Yerusalemu ku mibadwomibadwo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Koma ku Yudako kudzakhala anthu mpaka muyaya, ndipo ku Yerusalemu sikudzatha anthu pa mibadwo yonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Koma Yuda adzakhala ndi anthu mpaka muyaya ndi Yerusalemu ku mibadomibado.

Onani mutuwo Koperani




Yoweli 3:20
3 Mawu Ofanana  

Tayang'ana pa Ziyoni, mzinda wa zikondwerero zathu; maso ako adzaona, Yerusalemu malo a phee, chihema chimene sichidzasunthidwa, zichiri zake sizidzazulidwa konse, zingwe zake sizidzadulidwa.


Ndipo adzakhala m'dziko ndinalipereka kwa Yakobo mtumiki wanga, limene anakhalamo makolo anu, ndipo adzakhala m'mwemo iwo, ndi ana ao, ndi zidzukulu zao kosatha; ndi Davide mtumiki wanga adzakhala mtsogoleri wao kosatha.


Ndipo ndidzawaoka m'dziko mwao ndipo sadzazulidwanso m'dziko lao limene ndawapatsa, ati Yehova Mulungu wako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa