Yoweli 1:8 - Buku Lopatulika8 Lirani ngati namwali wodzimangira m'chuuno chiguduli, chifukwa cha mwamuna wa unamwali wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Lirani ngati namwali wodzimangira m'chuuno chiguduli, chifukwa cha mwamuna wa unamwali wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Inu anthu, lirani kwambiri ngati namwali wovala chiguduli. Wolira chifukwa cha imfa ya mnyamata wofuna kumkwatira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Lirani ngati namwali wovala chiguduli, chifukwa cha mwamuna wa utsikana wake. Onani mutuwo |