Yoweli 1:7 - Buku Lopatulika7 Unaonongadi mpesa wanga, nunyenya mkuyu wanga, nukungudza konse, nuutaya; nthambi zake zasanduka zotumbuluka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Unaonongadi mpesa wanga, nunyenya mkuyu wanga, nukungudza konse, nuutaya; nthambi zake zasanduka zotumbuluka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Aononga mpesa wanga, athyolathyola mitengo yanga ya mikuyu. Aisadza, aikungunula makungwa, naŵataya, nthambi zake nkumazisiya zili mbee. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Wawononga mphesa zanga ndipo wathyola mitengo yanga ya mkuyu. Wakungunula makungwa ake ndi kuwataya, kusiya nthambi zake zili mbee. Onani mutuwo |