Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yoweli 1:17 - Buku Lopatulika

17 Mbeu zaola pansi pa zibuluma zao; zosungiramo zaonongeka, nkhokwe zapasuka; pakuti tirigu wakwinyata.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Mbeu zaola pansi pa zibuluma zao; zosungiramo zaonongeka, nkhokwe zapasuka; pakuti tirigu wakwinyata.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Mbeu zakongonyala, poti pansi mpouma. Nyumba zosungiramo dzinthu zaonongeka, nkhokwe zapasuka, popeza kuti zokolola palibe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Mbewu zikunyala poti pansi ndi powuma. Nyumba zosungiramo zinthu zawonongeka; nkhokwe zapasuka popeza tirigu wauma.

Onani mutuwo Koperani




Yoweli 1:17
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu anamvera Efuroni, ndipo Abrahamu anamuyesera Efuroni ndalama zimene ananena alinkumva ana a Hiti, masekeli a siliva mazana anai, ndalama zomwezo agulana nazo malonda.


Yang'anirani mbalame za kumwamba, kuti sizimafesa ai, kapena sizimatema ai, kapena sizimatutira m'nkhokwe; ndipo Atate wanu wa Kumwamba azidyetsa. Nanga inu mulibe kusiyana nazo kuziposa kodi?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa