Yoweli 1:16 - Buku Lopatulika16 Chakudya sichichotsedwa kodi pamaso pathu? Chimwemwe ndi chikondwerero pa nyumba ya Mulungu wathu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Chakudya sichichotsedwa kodi pamaso pathu? Chimwemwe ndi chikondwerero pa nyumba ya Mulungu wathu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Chakudya chathu chikutha ife tikuwona. Mulibenso chimwemwe ndi chisangalalo m'Nyumba ya Mulungu wathu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Kodi chakudya chathu sichachotsedwa ife tikuona? Kodi mʼnyumba ya Mulungu wathu simulibe chimwemwe ndi chisangalalo? Onani mutuwo |