Yoweli 1:15 - Buku Lopatulika15 Kalanga ine, tsikuli! Pakuti layandikira tsiku la Yehova, lidzafika ngati chionongeko chochokera kwa Wamphamvuyonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Kalanga ine, tsikuli! Pakuti layandikira tsiku la Yehova, lidzafika ngati chionongeko chochokera kwa Wamphamvuyonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Kalanga ine! Tsiku loopsa layandikira, tsiku la Chauta, likubwera ndi chiwonongeko chochokera kwa Mphambe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Kalanga ine tsikulo! Pakuti tsiku la Yehova layandikira; lidzabwera ngati chiwonongeko chochokera kwa Wamphamvuzonse. Onani mutuwo |