Yoswa 9:3 - Buku Lopatulika3 Koma pamene nzika za Gibiyoni zinamva zimene Yoswa adachitira Yeriko ndi Ai, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Koma pamene nzika za Gibiyoni zinamva zimene Yoswa adachitira Yeriko ndi Ai, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono Ahivi a ku Gibiyoni atamva zimene Yoswa adaachita mzinda wa Yeriko ndi wa Ai, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Koma Ahivi ena a ku Gibiyoni atamva zomwe Yoswa anachitira mizinda ya Yeriko ndi Ai, Onani mutuwo |