Yoswa 9:4 - Buku Lopatulika4 zinachita momchenjerera, ndipo zinapita mooneka ngati mithenga, ndipo zinatenga matumba akale pa abulu ao, ndi matumba a vinyo akale ndi ong'ambika ndi omangamanga; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 zinachita momchenjerera, nizimuka nizioneka ngati mithenga, nizitenga matumba akale pa abulu ao, ndi matumba a vinyo akale ndi ong'ambika ndi omangamanga; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 adaganiza zoti amugwire m'maso. Adapita nasenzetsa abulu chakudya cha m'matumba akalekale, ndiponso matumba a vinyo a chikopa cha zigamba zokhazokha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 anaganiza zochita zachinyengo. Anapita nasenzetsa abulu awo chakudya mʼmatumba akalekale ndiponso matumba a vinyo achikopa ongʼambikangʼambika. Onani mutuwo |