Yoswa 9:2 - Buku Lopatulika2 anasonkhana kuponyana ndi Yoswa ndi Israele, ndi mtima umodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 anasonkhana kuponyana ndi Yoswa ndi Israele, ndi mtima umodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndiye onseŵa adapangana za kulimbana ndi Yoswa ndi Aisraele onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 anapangana kuti achite nkhondo ndi Yoswa ndi Israeli. Onani mutuwo |