Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 9:2 - Buku Lopatulika

2 anasonkhana kuponyana ndi Yoswa ndi Israele, ndi mtima umodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 anasonkhana kuponyana ndi Yoswa ndi Israele, ndi mtima umodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Ndiye onseŵa adapangana za kulimbana ndi Yoswa ndi Aisraele onse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 anapangana kuti achite nkhondo ndi Yoswa ndi Israeli.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 9:2
15 Mawu Ofanana  

Zoonadi, wochimwa sadzapulumuka chilango; koma mbeu ya olungama idzalanditsidwa.


Taona, iwo angasonkhanitse pamodzi, koma si ndi Ine; aliyense amene adzasonkhana pamodzi akangane ndi iwe adzagwa chifukwa cha iwe.


Musachinene, Chiwembu; chilichonse chimene anthu awa adzachinena, Chiwembu; musaope monga kuopa kwao kapena musachite mantha.


Pamenepo mafumu asanu a Aamori, ndiwo mfumu ya ku Yerusalemu, mfumu ya ku Hebroni, mfumu ya ku Yaramuti, mfumu ya ku Lakisi, mfumu ya ku Egiloni anasonkhana, nakwera iwo ndi makamu ao onse namanga misasa pa Gibiyoni, nauthira nkhondo.


Ndipo kunali, pamene Yabini mfumu ya ku Hazori anachimva, anatuma kwa Yobabu mfumu ya ku Madoni, ndi kwa mfumu ya ku Simironi, ndi kwa mfumu ya ku Akisafu,


Ndipo mafumu awa onse anasonkhana, nadza namanga pamodzi ku madzi a Meromu, kumthira Israele nkhondo.


Pamenepo munaoloka Yordani, ndi kufika ku Yeriko; ndi eni ake a ku Yeriko anaponyana nanu nkhondo, Aamori, ndi Aperizi, ndi Akanani, ndi Ahiti, ndi Agirigasi, Ahivi, ndi Ayebusi; ndipo ndinawapereka m'dzanja lanu.


pakuti ali mizimu ya ziwanda zakuchita zizindikiro; zimene zituluka kunka kwa mafumu a dziko lonse, kuwasonkhanitsira kunkhondo ya tsiku lalikulu la Mulungu, Wamphamvuyonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa