Yoswa 8:3 - Buku Lopatulika3 Pamenepo anauka Yoswa, ndi anthu onse a nkhondo, kuti akwere ku Ai; ndipo Yoswa anasankha amuna zikwi makumi atatu, ndiwo ngwazi, nawatumiza apite usiku, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pamenepo anauka Yoswa, ndi anthu onse a nkhondo, kuti akwere ku Ai; ndipo Yoswa anasankha amuna zikwi makumi atatu, ndiwo ngwazi, nawatumiza apite usiku, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Motero Yoswa adakonzeka ndi ankhondo ake kupita ku Ai. Adasankhula ankhondo ena olimba mtima zikwi makumi atatu, ndipo adaŵatuma usiku. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kotero Yoswa ndi gulu lonse la nkhondo anakonzeka kupita ku Ai. Iye anasankha amuna 30,000 odziwa kumenya nkhondo bwino ndipo anawatumiza usiku Onani mutuwo |