Yoswa 8:2 - Buku Lopatulika2 ndipo uzimchitira Ai ndi mfumu yake monga umo unamchitira Yeriko ndi mfumu yake; koma zofunkha zake ndi ng'ombe zake mudzifunkhire nokha; udziikire anthu alalire kukhonde kwa mzinda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 ndipo uzimchitira Ai ndi mfumu yake monga umo unamchitira Yeriko ndi mfumu yake; koma zofunkha zake ndi ng'ombe zake mudzifunkhire nokha; udziikire anthu alalire kukhonde kwa mudzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mzinda wa Ai ndi mfumu yake yomwe, muuchite zomwe mudachita Yeriko ndi mfumu yake. Koma katundu wamumzindamo ndi zoŵeta, musunge zikhale zanu. Muulalire mzindawo, ndipo muuthire nkhondo cha kumbuyo kwake.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mzinda wa Ai ndi mfumu yake muchite monga munachita ndi mzinda wa Yeriko ndi mfumu yake, koma katundu wa mumzindamo ndi zoweta mukazitenge ndi kuzisunga kuti zikhale zanu. Mukalalire mzinda wa Ai ndi kuwuthira nkhondo kuchokera kumbuyo.” Onani mutuwo |